Mas. 134 - Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kuuza anthu kuti atamande MulunguNyimbo yoimba pokwera ku Yerusalemu.

1Bwerani, mudzatamande Chauta,

Inu nonse atumiki a Chauta,

inu amene mumatumikira m'Nyumba mwake usiku.

2Kwezani manja anu popemphera m'malo ake oyera,

ndipo mutamande Chauta.

3Akudalitseni Chauta amene amakhala ku Ziyoni,

amene adalenga kumwamba ndi dziko lapansi.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help