1Ati kukoma ndi kukondweretsa ati,
anthu akakhala amodzi mwaubale!
2Ndi ngati mafuta amtengowapatali oĊµathira pa mutu,
otsikira ku ndevu, ku ndevu za Aroni,
oyenderera mpaka ku khosi la mkanjo wake.
3Ndi ngati mame a ku Heremoni,
omatsikira ku mapiri a Ziyoni.
Ku Ziyoni Chauta amaperekako madalitso,
ndiye kuti moyo wamuyaya.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.