Esr. 3 - Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14Mau a m'kalatayo ankayenera kudziŵika m'dera lililonse kuti ndi lamulo ndithu. Motero adayenera kuŵalengeza kwa anthu a mitundu yonse, kuti akonzekere pa tsiku limenelo.

15Anthu amtokoma aja adapita mofulumira, mfumu itaŵalamula, ndipo adapereka lamulo ku Susa, likulu la dziko. Tsono mfumu ndi Hamani adakhala pansi nkumamwa. Koma anthu a ku Susa adagwidwa ndi nthumanzi.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help