YAKOBO Mau Oyamba - Buku Lopatulika ndilo Mau a Mulungu

Mau OyambaWolemba kalatayi alembera Akhristu achiyuda obalalika kumaiko osiyanasiyana. Apereka malangizo amitundumitundu owathandiza kuwongolera moyo wao wa masiku onse mwa njira ya Chikhristu. Aziwonetsa makhalidwe abwino pa zochita zao zonse, pakuti “chikhulupiriro, chikapanda kukhala nacho ntchito, chikhala chakufa m'kati mwakemo.” (2.17)Za mkatimuMau oyamba 1.1Za chikhulupiriro ndi nzeru 1.2-8Za umphawi ndi chuma 1.9-11Za kuyesedwa ndi zovuta kapena zinyengo 1.12-18Za kumva ndi kuchita zimene Mulungu anena 1.19-27Awachenjeza kuti asamachite tsankho 2.1-13Za chikhulupiriro ndi ntchito zake 2.14-26Za kuwongolera lilime potsata nzeru zochokera kumwamba 3.1-18Za kuchita chibwenzi ndi pansi pano 4.1—5.6Za kuyembekeza mopirira ndi kupempherera odwala 5.7-20
Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help