MIYAMBO 7 - Buku Lopatulika ndilo Mau a Mulungu

Achenjere naye mkazi woipa

1Mwananga, sunga mau anga,

ukundike malangizo anga,

2

ndi chisiyo ndi sinamoni.

18Tiye tikondwere ndi chikondano mpaka mamawa;

tidzisangalatse ndi chiyanjano.

19Pakuti mwamuna kulibe kwathu,

wapita ulendo wa kutali;

20watenga thumba la ndalama m'dzanja lake,

tsiku lowala mwezi adzabwera kwathu.

21Amkakamiza ndi kukoka kwa mau ake,

ampatutsa ndi kusyasyalika kwa milomo yake.

22Mnyamatayo amtsata posachedwa,

monga ng'ombe ipita kukaphedwa;

ndi monga unyolo umadza kulanga chitsiru;

23 Mlal. 9.12 mpaka muvi ukapyoza mphafa yake;

amtsata monga mbalame yothamangira msampha;

osadziwa kuti adzaononga moyo wake.

24Ndipo tsopano, ananga, mundimvere ine,

labadirani mau a m'kamwa mwanga.

25Mtima wako usapatukire kunjira ya mkaziyo,

usasochere m'mayendedwe ake.

26 Neh. 13.26 Pakuti amagwetsa ambiri, atawalasa;

ndipo ophedwa ndi iye achulukadi.

27Nyumba yake ndiyo njira ya kumanda,

yotsikira kuzipinda za imfa.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help