NAHUMU Mau Oyamba - Buku Lopatulika ndilo Mau a Mulungu

Mau OyambaBukuli ndi ndakatulo yokondwerera kupasuka kwa Ninive, mzinda waukulu wa Aasiriya amene ankazunza Aisraele kuyambira kale. Kupasuka kwa mzindawo kuwoneka ngati chilango cha Mulungu chogwera anthu onyada ndi ankhanza.Za mkatimuChauta aimba Ninive mlandu 1.1-15

Kupasuka kwa mzindawo 2.1—3.19

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help