MASALIMO 134 - Buku Lopatulika ndilo Mau a Mulungu

Afulumizidwa anthu kulemekeza YehovaNyimbo yokwerera.

1 1Mbi. 9.33 Taonani, lemekezani Yehova, atumiki a Yehova inu nonse,

akuimirira m'nyumba ya Yehova usiku.

2 1Tim. 2.8 Kwezani manja anu kumalo oyera,

nimulemekeze Yehova.

3 Mas. 128.5 Yehova, ali mu Ziyoni, akudalitseni;

ndiye amene analenga kumwamba ndi dziko lapansi.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help