MASALIMO 131 - Buku Lopatulika ndilo Mau a Mulungu

Kudzichepetsa kwa Davide pakupempheraNyimbo yokwerera; ya Davide.

1 Aro. 12.16 Yehova, mtima wanga sunadzikuze

ndi maso anga sanakwezeke;

ndipo sindinatsate zazikulu,

kapena zodabwitsa zondiposa.

2 Mat. 18.3; 1Ako. 14.20 Indedi, ndinalinganiza ndi kutontholetsa moyo wanga;

ngati mwana womletsa kuyamwa amake,

moyo wanga ndili nao ngati mwana womletsa kuyamwa.

3Israele, uyembekezere Yehova,

kuyambira tsopano kufikira kosatha.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help