LEVITIKO Mau Oyamba - Buku Lopatulika ndilo Mau a Mulungu

Mau OyambaBuku la Levitiko likukamba za malamulo a chipembedzo ndi miyambo yosiyanasiyana mu Israele wakale, komanso za malamulo okhudza ansembe amene anali ndi udindo woonetsetsa kuti malamulowo akutsatidwa bwino lomwe.Mutu waukulu mu bukuli ndiwakuti Yehova ndi Woyera ndipo anthu ake ayenera kukhala oyera mtima pa kupembedza kwao ndiponso moyo wao onse kuti ubale wao ndi Mulungu usasokonezeke.Mau amene amadziwika bwino kuchokera mu bukuli ndi omwe Yesu adawanena kuti ndilo lamulo lachiwiri lalikulu: “Udzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini.” (19.18)Za mkatimuMalamulo onena za zopereka ndi nsembe 1.1—7.38

Aroni ndi ana ake awadzoza kukhala ansembe 8.1—10.20

Malamulo onena za mwambo wa kuyeretsedwa ndi kudetsedwa 11.1—15.33

Za tsiku lotetezera 16.1-34

Malamulo onena za chiyero pa moyo ndi pa chipembedzo 17.1—27.34

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help