YUDA Mau Oyamba - Buku Lopatulika Bible 2014

Mau Oyamba Kalata yolembedwa ndi mtumwi Yuda analembedwa pofuna kuwachenjeza za aphunzitsi onyenga amene amadzitcha okhulupirira. Mkalata iyi yachidule imene nkhani zake zikufanana ndi za mu Kalata yachiwiri yolembedwa ndi mtumwi Petro, ndipo wolembayo akuwalimbikitsa awerengi ake kuti “mulimbanetu chifukwa cha chikhulupiriro chapatsidwa kamodzi kwa oyera mtima”.Za mkatimuMau oyamba 1.1-2Khalidwe labwino, chiphunzitso, ndi mathero a aphunzitsi onyenga 1.3-16Awalimbikitsa asunge chikhulupiriro 1.17-23Mdalitso 1.24-25
Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help