1Mwenzi utakhala ngati mlongo wanga,
woyamwa pa bere la amai!
Ndikadakupeza panja, ndikadakupsompsona;
osandinyoza munthu.
2Ndikadakutsogolera, kukulowetsa m'nyumba ya amai,
kuti andilange mwambo;
ndikadakumwetsa vinyo wokoleretsa,
ndi madzi a makangaza anga.
3Dzanja lamanzere lake akadanditsamiritsa kumutu,
lamanja lake ndi kundifungatira.
4Ndikulumbirirani, ana akazi inu a ku Yerusalemu,
muutsiranji, mugalamutsiranji chikondi,
chisanafune mwini.
5
Ngati ndiye chitseko tidzamtsekereza ndi matabwa amikungudza.
10Ndine khoma, mawere anga akunga nsanja zake:
Pamaso pa mnyamatayo ndinafanana ngati wopeza mtendere.
11Solomoni anali ndi munda wamipesa ku Baala-Hamoni;
nabwereka alimi mundawo;
yense ambwezere ndalama chikwi chifukwa cha zipatso zake.
12Koma munda wanga wamipesa,
uli pamaso panga ndiwo wangatu;
nacho chikwicho, Solomoni iwe,
koma olima zipatso zake azilandira mazana awiri.
13Namwaliwe wokhala m'minda,
anzako amvera mau ako:
Nanenanso undimvetse.
14 Chiv. 22.17, 20 Dzifulumira, mnyamatawe wokondedwa wanga,
dzifanane ngati mphoyo pena mwana wa mbawala
pa mapiri a mphoka.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.