1Monga chipale chofewa m'malimwe, ndi mvula m'masika,
momwemo ulemu suyenera chitsiru.
2Monga mpheta ilikuzungulira, ndi namzeze alikuuluka,
momwemo temberero la pachabe silifikira.
3
24Wakuda mnzake amanyenga ndi milomo yake;
koma akundika chinyengo m'kati mwake.
25 Yer. 9.8 Pamene akometsa mau ake usamkhulupirire;
pakuti m'mtima mwake muli zonyansa zisanu ndi ziwiri.
26Angakhale abisa udani wake pochenjera,
koma udyo wake udzavumbulutsidwa posonkhana anthu.
27 Mas. 7.15-16; Mlal. 10.8 Wokumba dzenje adzagwamo,
wogubuduza mwala, udzabweranso pa iye mwini.
28Lilime lonama lida omwewo linawasautsa;
ndipo m'kamwa mosyasyalika mungoononga.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.