1 TIMOTEO 1 - Buku Lopatulika Bible 2014

Paulo alangiza Timoteo

1

18 1Tim. 4.14 Lamulo ili ndipereka kwa iwe, mwana wanga Timoteo, kuti, monga mwa zonenera zidakutsogolera iwe kale, ulimbane nayo nkhondo yabwino;

191Tim. 3.9; 6.9ndi kukhala nacho chikhulupiriro ndi chikumbu mtima chokoma, chimene ena adachikankha, chikhulupiriro chao chidatayika;

201Ako. 5.5; 2Tim. 4.14a iwo ali Himeneo ndi Aleksandro, amene ndawapereka kwa Satana, kuti aphunzire kusalankhula zamwano.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help