1Yehova, kumbukirani Davide
kuzunzika kwake konse.
2
analikhumba likhale pokhala pake; ndi kuti,
14Pampumulo panga mpano posatha,
Pano ndidzakhala; pakuti ndakhumbapo.
15 Mas. 147.14 Ndidzadalitsatu chakudya chake;
aumphawi ake ndidzawakhutitsa ndi mkate.
16Ndipo ansembe ake ndidzawaveka ndi chipulumutso:
Ndi okondedwa ake adzafuulitsa mokondwera.
17 1Maf. 11.36; Luk. 1.69 Apo ndidzaphukitsira Davide nyanga;
ndakonzeratu wodzozedwa wanga nyali.
18 Mas. 35.26 Ndidzawaveka adani ake ndi manyazi;
koma pa iyeyu korona wake adzamveka.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.