MASALIMO 132 - Buku Lopatulika Bible 2014

Davide asamalira Kachisi ndi likasa. Lonjezano la MulunguNyimbo yokwerera.

1Yehova, kumbukirani Davide

kuzunzika kwake konse.

2

analikhumba likhale pokhala pake; ndi kuti,

14Pampumulo panga mpano posatha,

Pano ndidzakhala; pakuti ndakhumbapo.

15 Mas. 147.14 Ndidzadalitsatu chakudya chake;

aumphawi ake ndidzawakhutitsa ndi mkate.

16Ndipo ansembe ake ndidzawaveka ndi chipulumutso:

Ndi okondedwa ake adzafuulitsa mokondwera.

17 1Maf. 11.36; Luk. 1.69 Apo ndidzaphukitsira Davide nyanga;

ndakonzeratu wodzozedwa wanga nyali.

18 Mas. 35.26 Ndidzawaveka adani ake ndi manyazi;

koma pa iyeyu korona wake adzamveka.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help