1
tinakhala ngati anthu akulota.
2
Yehova anawachitira iwo zazikulu.
3Yehova anatichitira ife zazikulu;
potero tikhala okondwera.
4Bwezani ukapolo wathu, Yehova,
ngati mitsinje ya kumwera.
5 Yer. 31.9-14 Akubzala ndi misozi adzatuta ndi kufuula mokondwera.
6Iye amene ayendayenda nalira, ponyamula mbeu yakufesa;
adzabweranso ndithu ndi kufuula mokondwera,
alikunyamula mitolo yake.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.