MASALIMO 18 - Buku Lopatulika Bible 2014

Nyimbo yoyamikira Yehova ya Davide(2Sam. 22)Kwa Mkulu wa Nyimbo. Salimo la Davide, mtumiki wa Yehova, amene ananena kwa Yehova mau a nyimbo iyi m'mene Yehova anamlanditsa m'dzanja la adani ake onse, ndi m'dzanja la Saulo: ndipo anati,

1

mtundu wa anthu sindinaudziwa udzanditumikira.

44Pakumva m'khutu za ine adzandimvera,

alendo adzandigonjera monyenga.

45Alendo adzafota,

nadzatuluka monjenjemera m'ngaka mwao.

46Yehova ngwa moyo; ndipo lidalitsike thanthwe langa;

nakwezeke Mulungu wa chipulumutso changa.

47Ndiye Mulungu amene andibwezerera chilango,

nandigonjetsera mitundu ya anthu.

48Andipulumutsa kwa adani anga.

Inde mundikweza pa iwo akundiukira ine,

mundikwatula kwa munthu wachiwawa.

49Chifukwa chake Yehova ndidzakuyamikani mwa amitundu,

ndipo dzina lanu ndidzaliimbira.

50 2Sam. 7.13, 29; Mas. 144.10 Alanditsa mfumu yake ndi chipulumutso chachikulu;

nachitira chifundo wodzozedwa wake,

Davide, ndi mbumba yake, kunthawi zonse.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help