3 YOHANE Mau Oyamba - Buku Lopatulika Bible 2014

Mau Oyamba Kalata yachitatu yolembedwa ndi mtumwi Yohane inalembedwa ndi “Mkuluyo” kulembera mtsogoleri wa mpingo dzina lake Gayo. Mlembiyo akumuyamikira Gayo chifukwa cha kuthandiza akhristu ena, komanso akuwachenjeza za munthu wina dzina lake Diotrefe.Za mkatimuMau oyamba 1.1-4Gayo akumulemekeza 1.5-8Diotrefe akumudzudzula 9-10Demetrio akumuyamikira 1.11-12Mau omaliza 1.13-15
Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help