HABAKUKU 3 - Buku Lopatulika Bible 2014

Pemphero la Habakuku

1Pemphero la Habakuku mneneri, pa Sigionoti.

2

ndi mapiri achikhalire anamwazika,

zitunda za kale lomwe zinawerama;

mayendedwe ake ndiwo a kale lomwe.

7Ndinaona mahema a Kusani ali mkusauka;

nsalu zotchinga za dziko la Midiyani zinanjenjemera.

8Kodi Yehova anaipidwa nayo mitsinje?

Mkwiyo wanu unali pamitsinje kodi,

kapena ukali wanu panyanja,

kuti munayenda pa akavalo anu,

pa magaleta anu a chipulumutso?

9

ndi m'minda m'mosapatsa chakudya;

ndi zoweta zachotsedwa kukhola,

palibenso ng'ombe m'makola mwao;

18 Yob. 13.15; Yes. 61.10 koma ndidzakondwera mwa Yehova,

ndidzasekerera mwa Mulungu wa chipulumutso changa.

19 Mas. 27.1 Yehova, Ambuye, ndiye mphamvu yanga,

asanduliza mapazi anga ngati a mbawala,

nadzandipondetsa pa misanje yanga.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help