1
3Yerusalemu anamangidwa
ngati mudzi woundana bwino:
4 Deut. 16.16 Kumene akwerako mafuko, ndiwo mafuko a Yehova;
akhale mboni ya kwa Israele, Ayamike dzina la Yehova.
5 2Mbi. 19.8 Pakuti pamenepo anaika mipando ya chiweruzo,
mipando ya nyumba ya Davide.
6 Yer. 29.7 Mupempherere mtendere wa Yerusalemu;
akukonda inu adzaona phindu.
7M'linga mwako mukhale mtendere,
m'nyumba za mafumu mukhale phindu.
8Chifukwa cha abale anga ndi mabwenzi anga,
ndidzanena tsopano, Mukhale mtendere mwa inu.
9 Neh. 2.10 Chifukwa cha nyumba ya Yehova Mulungu wathu
ndidzakufunira zokoma.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.