MARKO 15 - Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu aweruzidwa ndi Pilato(Mat. 27.1-2, 11-31; Luk. 23.1-25; Yoh. 18.28—19.16)

1

29Yesu aikidwa m'manda(Mat. 27.57-66; Luk. 23.50-56; Yoh. 19.38-42)

42Ndipo atafika tsono madzulo, popeza mpa tsiku lokonzekera, ndilo la pambuyo pa Sabata,

43Luk. 2.25, 38anadzapo Yosefe wa ku Arimatea, mkulu wa milandu womveka, amene yekha analikuyembekezera Ufumu wa Mulungu; nalimba mtima nalowa kwa Pilato, napempha mtembo wake wa Yesu.

44Ndipo Pilato anazizwa ngati adamwaliradi; naitana kenturiyo, namfunsa ngati adamwalira kale.

45Ndipo pamene anachidziwa ndi kenturiyo, anamninkha Yosefe mtembowo.

46Luk. 23.53Ndipo anagula bafuta, namtsitsa Iye, namkulunga m'bafutamo, namuika m'manda osemedwa m'thanthwe; nakunkhunizira mwala pakhomo la manda.

47Ndipo Maria wa Magadala ndi Maria amake wa Yosefe anapenya pomwe anaikidwapo.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help