2 SAMUELE 22 - Buku Lopatulika Bible 2014

Nyimbo yoyamikira Yehova ya Davide(Mas. 18)

1

Anthu amene sindinawadziwa adzanditumikira ine.

45Alendo adzandigonjera ine,

pakumva za ine, adzandimvera pomwepo.

46Alendo adzafota,

nadzabwera ndi kunthunthumira otuluka mokwiririka mwao.

47 Eks. 15.2 Yehova ali ndi moyo; ndipo lidalitsike thanthwe langa;

ndipo akulitsidwe Mulungu wa thanthwe la chipulumutso changa;

48inde Mulungu wakundibwezera chilango ine,

ndi kundigonjetsera anthu a mitundu.

49Amene anditulutsa kwa adani anga;

inde mundikweza ine pamwamba pa iwo akundiukira;

mundipulumutsa kwa munthu wachiwawa.

50 Aro. 15.9 Chifukwa chake ndidzakuongani Yehova, pakati pa amitundu,

ndipo ndidzaimba zolemekeza dzina lanu.

51 Mas. 89.20, 29 Iye apatsa mfumu yake chipulumutso chachikulu;

naonetsera chifundo wodzozedwa wake,

kwa Davide ndi mbeu yake ku nthawi zonse.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help