1
opikisana ndi Iye asadzikuze.
8Lemekezani Mulungu wathu, mitundu ya anthu inu,
ndipo mumveketse liu la chilemekezo chake.
9
11Munapita nafe kuukonde;
munatisenza chothodwetsa pamsana pathu.
12 Yes. 43.2 Munapititsa anthu oberekeka pamwamba pamitu pathu;
tinapyola moto ndi madzi;
koma munatifikitsa potitsitsimutsa.
13Ndidzalowa m'nyumba yanu ndi nsembe zopsereza,
ndidzakuchitirani zowinda zanga,
14zimene inazitchula milomo yanga,
ndinazinena pakamwa panga posautsika ine.
15Ndidzakufukizirani nsembe zopsereza zonona,
pamodzi ndi chofukiza cha mphongo za nkhosa;
ndidzakonza ng'ombe pamodzi ndi mbuzi.
16 Mas. 34.11 Idzani, imvani, inu nonse akuopa Mulungu,
ndipo ndidzafotokozera zonse anazichitira moyo wanga.
17Ndinamfuulira Iye pakamwa panga,
ndipo ndinamkuza ndi lilime langa.
18 Miy. 28.9; Yoh. 9.31; Yak. 4.3 Ndikadasekera zopanda pake m'mtima mwanga,
Ambuye sakadamvera.
19 Mas. 116.1-2 Koma Mulungu anamvadi;
anamvera mau a pemphero langa.
20Wolemekezeka Mulungu,
amene sanandipatutsire ine pemphero langa,
kapena chifundo chake.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.