MASALIMO 66 - Buku Lopatulika Bible 2014

Achenjeza onse alemekeze Mulungu pa ntchito zake zodabwitsaKwa Mkulu wa Nyimbo. Nyimbo, Salimo.

1

opikisana ndi Iye asadzikuze.

8Lemekezani Mulungu wathu, mitundu ya anthu inu,

ndipo mumveketse liu la chilemekezo chake.

9

11Munapita nafe kuukonde;

munatisenza chothodwetsa pamsana pathu.

12 Yes. 43.2 Munapititsa anthu oberekeka pamwamba pamitu pathu;

tinapyola moto ndi madzi;

koma munatifikitsa potitsitsimutsa.

13Ndidzalowa m'nyumba yanu ndi nsembe zopsereza,

ndidzakuchitirani zowinda zanga,

14zimene inazitchula milomo yanga,

ndinazinena pakamwa panga posautsika ine.

15Ndidzakufukizirani nsembe zopsereza zonona,

pamodzi ndi chofukiza cha mphongo za nkhosa;

ndidzakonza ng'ombe pamodzi ndi mbuzi.

16 Mas. 34.11 Idzani, imvani, inu nonse akuopa Mulungu,

ndipo ndidzafotokozera zonse anazichitira moyo wanga.

17Ndinamfuulira Iye pakamwa panga,

ndipo ndinamkuza ndi lilime langa.

18 Miy. 28.9; Yoh. 9.31; Yak. 4.3 Ndikadasekera zopanda pake m'mtima mwanga,

Ambuye sakadamvera.

19 Mas. 116.1-2 Koma Mulungu anamvadi;

anamvera mau a pemphero langa.

20Wolemekezeka Mulungu,

amene sanandipatutsire ine pemphero langa,

kapena chifundo chake.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help