2 MBIRI Mau Oyamba - Buku Lopatulika Bible 2014

Mau OyambaBukuli likamba za mfumu Solomoni ndi mafumu a ku Yuda okha mpaka nthawi ya kupasuka kwa mzinda wa Yerusalemu.Za mkatimuUfumu wa Solomoni 1.1—9.31

a. Zaka zoyamba za ufumu wake 1.1-17

b. Amanga Kachisi wa Yehova 2.1—7.10

c. Zaka zotsiriza za ufumu wake 7.11—9.31

Za mafumu ena a ku Yuda 10.1—36.23

a. Mafumu akumpoto aukira ufumu wa Rehobowamu 10.1-19

b. Mafumu a ku Yuda 11.1—36.12

c. Kupasuka kwa mzinda wa Yerusalemu 36.13-23

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help