MASALIMO 100 - Buku Lopatulika Bible 2014

Olengedwa ndi Mulungu amlemekezeSalimo la Chiyamiko.

1 Mas. 95.1 Fuulirani kwa Yehova, inu, dziko lonse lapansi.

2Tumikirani Yehova ndi chikondwerero:

Idzani pamaso pake ndi kumuimbira mokondwera.

3 Gen. 1.26; Mas. 95.7; Ezk. 34.30-31; Aef. 2.10 Dziwani kuti Yehova ndiye Mulungu;

Iyeyu anatilenga, ndipo ife ndife ake;

ndife anthu ake ndi nkhosa zapabusa pake.

4 Mas. 66.13 Lowani kuzipata zake ndi chiyamiko,

ndi kumabwalo ake ndi chilemekezo:

Myamikeni; lilemekezeni dzina lake.

5 Mas. 136.1-26 Pakuti Yehova ndiye wabwino;

chifundo chake chimanka muyaya;

ndi chikhulupiriko chake ku mibadwomibadwo.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help