AFILIPI 4 - Buku Lopatulika Bible 2014

1

8Chotsalira, abale, zinthu zilizonse zoona, zilizonse zolemekezeka, zilizonse zolungama, zilizonse zoyera, zilizonse zokongola, zilizonse zimveka zokoma; ngati kuli chokoma mtima china, kapena chitamando china, zilingirireni izi.

9

21 Agal. 1.2 Lankhulani woyera mtima aliyense mwa Khristu Yesu. Abalewo akukhala ndi ine alankhula inu.

22Afi. 1.13Oyera mtima onse alankhula inu, koma makamaka iwo a banja la Kaisara.

23Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi mzimu wanu.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help