YOBU 15 - Buku Lopatulika Bible 2014

Elifazi atsutsa Yobu pa kudzikuza kwake. Akuti, akulu omwe atsimikiza kuti ochimwa sakhala bwino

1Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,

2Kodi mwini nzeru ayankhe ndi kudziwa kouluzika,

ndi kudzaza mimba yake ndi mphepo ya kum'mawa?

3Kodi atsutsane ndi mnzake ndi mau akusathandiza?

Kapena ndi maneno akusaphindulitsa?

4Zedi uyesa chabe mantha,

nuchepsa chilingiriro pamaso pa Mulungu.

5Pakuti pakamwa pako paphunzitsa mphulupulu zako,

nusankha lilime la ochenjerera.

6

34Pakuti msonkhano wa onyoza Mulungu udzakhala chumba,

ndi moto udzapsereza mahema a olandira chokometsera mlandu.

35 Mas. 7.14 Aima ndi chovuta, nabala mphulupulu,

ndi m'mimba mwao mukonzeratu chinyengo.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help