MASALIMO 33 - Buku Lopatulika Bible 2014

Alemekeza Mulungu wolenga, wosunga zonse

1

asandutsa chabe zolingirira za mitundu ya anthu.

11 Yes. 46.10 Chiweruzo cha Yehova chikhazikika chikhazikikire,

zolingirira za m'mtima mwake ku mibadwomibadwo.

12 Mas. 144.15 Wodalitsika mtundu wa anthu

umene Yehova ndiye Mulungu wao;

mtundu womwe anausankha ukhale cholandira cha Iye yekha.

13Yehova apenyerera m'mwamba;

aona ana onse a anthu.

14M'malo akhalamo Iye, amapenya pansi

pa onse akukhala m'dziko lapansi.

15 Yer. 32.19 Iye amene akonza mitima ya iwo onse,

amene azindikira zochita zao zonse.

16 Mas. 44.6 Palibe mfumu yoti gulu lalikulu limpulumutsa,

mphamvu yaikulu siichilanditsa chiphona.

17 Miy. 21.31 Kavalo safikana kupulumuka naye,

chinkana mphamvu yake njaikulu sapulumutsa.

18 Mas. 34.15 Taonani, diso la Yehova lili pa iwo akumuopa Iye,

pa iwo akuyembekeza chifundo chake.

19Kupulumutsa moyo wao kwa imfa,

ndi kuwasunga ndi moyo m'nyengo ya njala.

20 Mas. 62.1, 5 Moyo wathu walindira Yehova;

Iye ndiye thandizo lathu ndi chikopa chathu.

21 Yoh. 16.22 Pakuti mtima wathu udzakondwera mwa Iye,

chifukwa takhulupirira dzina lake loyera.

22Yehova, chifundo chanu chikhale pa ife,

monga takuyembekezani Inu.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help