1 PETRO 5 - Buku Lopatulika Bible 2014

Zoyenera akulu ndi anyamata; adzichepetse, adikire

1

12 1Ako. 15.1; 2Ako. 1.19 Mwa Silivano, mbale wathu wokhulupirika monga ndimayesa, ndalembera kwa inu mwachidule, ndi kudandaulira, ndi kuchita umboni, kuti chisomo choona cha Mulungu ndi ichi; m'chimenechi muimemo.

13Mac. 12.12, 25Iye wa ku Babiloni wosankhidwa pamodzi nanu akulankhulani; ateronso Marko mwana wanga.

14Aro. 16.16; Aef. 6.23Mupatsane moni ndi chipsompsono cha chikondi.

Mtendere ukhale ndi inu nonse muli mwa Khristu.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help