MASALIMO 102 - Buku Lopatulika Bible 2014

Wopsinjika apempha Mulungu achitire anthu ake chifundo, amitundu nammverensoPemphero la Wozunzika, m'mene anakomoka natsanulira cholingalira chake pamaso pa Yehova.

1Yehova, imvani pemphero langa,

ndipo mfuu wanga ufikire Inu.

2

popeza yafika nyengo yakumchitira chifundo, nyengo yoikika.

14Pakuti atumiki anu akondwera nayo miyala yake,

nachitira chifundo fumbi lake.

15

22Posonkhana pamodzi mitundu ya anthu,

ndi maufumu kuti atumikire Yehova.

23Iye analanda mphamvu yanga panjira;

anachepsa masiku anga.

24 Yes. 38.10 Ndinati, Mulungu wanga, musandichotse pakati pa masiku anga:

Zaka zanu zikhalira m'mibadwomibadwo.

25 Gen. 1.1; 2.1; Aheb. 1.10-12 Munakhazika dziko lapansi kalelo;

ndipo zakumwamba ndizo ntchito ya manja anu.

26 Aheb. 1.10-12 Zidzatha izi, koma Inu mukhala:

Inde, zidzatha zonse ngati chovala;

mudzazisintha ngati malaya, ndipo zidzasinthika:

27 Mala. 3.6; Aheb. 13.8 Koma Inu ndinu yemweyo,

ndi zaka zanu sizifikira kutha.

28 Mas. 69.36 Ana a atumiki anu adzakhalitsa,

ndi mbeu zao zidzakhazikika pamaso panu.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help