1Yehova, imvani pemphero langa,
ndipo mfuu wanga ufikire Inu.
2
popeza yafika nyengo yakumchitira chifundo, nyengo yoikika.
14Pakuti atumiki anu akondwera nayo miyala yake,
nachitira chifundo fumbi lake.
15
22Posonkhana pamodzi mitundu ya anthu,
ndi maufumu kuti atumikire Yehova.
23Iye analanda mphamvu yanga panjira;
anachepsa masiku anga.
24 Yes. 38.10 Ndinati, Mulungu wanga, musandichotse pakati pa masiku anga:
Zaka zanu zikhalira m'mibadwomibadwo.
25 Gen. 1.1; 2.1; Aheb. 1.10-12 Munakhazika dziko lapansi kalelo;
ndipo zakumwamba ndizo ntchito ya manja anu.
26 Aheb. 1.10-12 Zidzatha izi, koma Inu mukhala:
Inde, zidzatha zonse ngati chovala;
mudzazisintha ngati malaya, ndipo zidzasinthika:
27 Mala. 3.6; Aheb. 13.8 Koma Inu ndinu yemweyo,
ndi zaka zanu sizifikira kutha.
28 Mas. 69.36 Ana a atumiki anu adzakhalitsa,
ndi mbeu zao zidzakhazikika pamaso panu.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.