1Taona, wakongola, bwenzi langa,
namwaliwe, taona, wakongola;
maso ako akunga a nkhunda patseri pa chophimba chako.
Tsitsi lako likunga gulu la mbuzi,
zooneka pa phiri la Giliyadi.
2Mano ako akunga gulu la nkhosa zosengasenga,
zokwera kuchokera kosamba;
yonse ili ndi ana awiri,
palibe imodzi yopoloza.
3Milomo yako ikunga mbota yofiira,
m'kamwa mwako ndi kukoma:
Palitsipa pako pakunga phande la khangaza
paseli pa chophimba chako.
4
ndi kuchitunda cha lubani.
7
14Narido ndi chikasu,
nzimbe ndi sinamoni, ndi mitengo yonse ya lubani;
mure ndi khonje, ndi zonunkhiritsa zonse zomveka.
15 Yes. 49.10; Yoh. 4.10 Ndiwe kasupe wa m'minda,
chitsime cha madzi amoyo,
ndi mitsinje yoyenda yochokera ku Lebanoni.
Ayankha mkwatibwi16Galamuka, mphepo ya kumpoto iwe,
nudze, mphepo iwe ya kumwera;
nuombe pamunda panga, kuti zonunkhiritsa zake zitulukemo.
Bwenzi langa mnyamatayo, alowe m'munda mwake,
nadye zipatso zake zofunika.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.