ESTERE Mau Oyamba - Buku Lopatulika Bible 2014

Mau OyambaBukuli likukamba za Estere, mtsikana wina wachiyuda, amene ankakonda kwambiri anthu a mtundu wake, naonetsa kulimba mtima kwake pothandiza kuwapulumutsa Ayudawo kwa adani ao. Lifotokozanso za chiyambi chake komanso tanthauzo la chikondwerero cha Chiyuda chotchedwa Purimu.Za mkatimuEstere asankhidwa kuti akhale mfumukazi kudziko la Persiya 1.1—2.23

Hamani apanga chiwembu chifuna kuwonongeratu fuko la Ayuda 3.1—5.14

Hamani atsutsidwa naphedwa 6.1—7.10

Ayuda agonjetsa adani ao 8.1—10.3

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help