2 YOHANE Mau Oyamba - Buku Lopatulika Bible 2014

Mau Oyamba Kalata yachiwiri yolembedwa ndi mtumwi Yohane inalembedwa ndi “Mkuluyo” kupita kwa “mkazi womveka wosankhika, ndi ana ake”, amene mwina akutanthauza mpingo ndi anthu ake. Uthenga wake ndi waufupi ndipo ndi wolimbitsana za kukondana komanso kuchenjeza za aphunzitsi onyenga ndi ziphunzitso zawo zachinyengo.Za mkatimuMau oyamba 1.1-3Kufunikira kwa chikondi 1.4-6Awachenjeze asatsate ziphunzitso zonyenga 1.7-11Mau omaliza 1.12-13
Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help