NYIMBO YA SOLOMONI 3 - Buku Lopatulika Bible 2014

Mkwatibwi apeza mkwati

1

pali mphoyo, ndi mbawala ya kuthengo,

kuti musautse, ngakhale kugalamutsa chikondi,

mpaka chikafuna mwini.

Ulendo wa ukwati

6

ndi zonunkhiritsa zonse za wogulitsa?

7Taonani, ndi machila a Solomoni;

pazingapo amuna amphamvu makumi asanu ndi limodzi,

a mwa ngwazi za Israele.

8Onsewo agwira lupanga, nazolowera nkhondo:

Yense ali ndi lupanga lake pantchafu pake,

chifukwa cha upandu wa usiku.

9Solomoni mfumu anadzipangira machila okhalamo tsonga

ndi matabwa a ku Lebanoni.

10Anapanga timilongoti take ndi siliva,

cha pansi pake ndi golide, mpando wake ndi nsalu yofiirira,

pakati pake panayalidwa za chikondi

cha ana akazi a ku Yerusalemu.

11Tulukani, ana akazi inu a Ziyoni,

mupenye Solomoni mfumu,

ndi korona amake amamveka naye tsiku la ukwati wake,

ngakhale tsiku lakukondwera mtima wake.

Blog
About Us
Message
Site Map

Who We AreWhat We EelieveWhat We Do

Terms of UsePrivacy Notice

2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.

Home
Gospel
Question
Blog
Help