1
pali mphoyo, ndi mbawala ya kuthengo,
kuti musautse, ngakhale kugalamutsa chikondi,
mpaka chikafuna mwini.
Ulendo wa ukwati6
ndi zonunkhiritsa zonse za wogulitsa?
7Taonani, ndi machila a Solomoni;
pazingapo amuna amphamvu makumi asanu ndi limodzi,
a mwa ngwazi za Israele.
8Onsewo agwira lupanga, nazolowera nkhondo:
Yense ali ndi lupanga lake pantchafu pake,
chifukwa cha upandu wa usiku.
9Solomoni mfumu anadzipangira machila okhalamo tsonga
ndi matabwa a ku Lebanoni.
10Anapanga timilongoti take ndi siliva,
cha pansi pake ndi golide, mpando wake ndi nsalu yofiirira,
pakati pake panayalidwa za chikondi
cha ana akazi a ku Yerusalemu.
11Tulukani, ana akazi inu a Ziyoni,
mupenye Solomoni mfumu,
ndi korona amake amamveka naye tsiku la ukwati wake,
ngakhale tsiku lakukondwera mtima wake.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.