1
Ndidzayamika Yehova ndi mtima wonse,
mu upo wa oongoka mtima, ndi mumsonkhano.
2
7 Mas. 19.9 Ntchito za manja ake ndizo choonadi ndi chiweruzo;
malangizo ake onse ndiwo okhulupirika.
8 Mat. 5.18 Achirikizika kunthawi za nthawi,
achitika m'choonadi ndi chilunjiko.
9 Mat. 1.21; Luk. 1.49 Anatumizira anthu ake chipulumutso;
analamulira chipangano chake kosatha;
dzina lake ndilo loyera ndi loopedwa.
10 Deut. 4.5-6; Miy. 1.7 Kumuopa Yehova ndiko chiyambi cha nzeru;
onse akuchita chotero ali nacho chidziwitso chokoma;
chilemekezo chake chikhalitsa kosatha.
Who We AreWhat We EelieveWhat We Do
2025 by iamachristian.org,Inc All rights reserved.